Angozo lyrics by Piksy - original song full text. Official Angozo lyrics, 2024 version | LyricsMode.com
Request & respond explanations
  • Don't understand the meaning of the song?
  • Highlight lyrics and request an explanation.
  • Click on highlighted lyrics to explain.
Piksy – Angozo lyrics
CHORUS
Angozo
Safuna zoyambana Angozo
Angozo
Safuna zokangana Angozo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ndi ntondo ntondo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ntondo

PIKSY
Wodya zake alibe mulandu
Ali ndi tsoka wopanga za anthu
Zawo zikuyenda
Nsanje ndi matenda
Zawo amanena ndi anthu Angozo ndi ofewa
Angozo sadzatheka
Humble, selfless
Sathoka za udolo wawo,
Ndi katundu, Amfumu
Koma mmudzimu akulemera ndani?
(Ndi Angozo)
Akazi abwino amagomera ndani?
(Angozo)
Pakati pawo alibe stress ndani?
(Ndi Angozo)
Ndekuti awa angochedwa kupanga ziphokoso
I am the definition of Angozo
Chikhala nyerere you know bwenzi ndiri mdzodzo
Tsono dzimakomo kutseguka
Chikho chawo kusefuka
Zowapinga kupatuka
Ineyo ndi Angozo

CHORUS
Angozo
Safuna zoyambana Angozo
Angozo
Safuna zokangana Angozo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ndi ntondo ntondo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ntondo

TAY GRIN
Angozo mdi bad man
Wa pa easy koma otchuka ngati Gangnam
Ndi ma chick amahita ngati Van Dame
Sadzipopa ngati bubble gum
Mfana ozitsata (ingofunsafunsa akuuza)
Mfana ozisanja (Ona Motor akuphusha)
Mfana wa chikoka (Anthu onse mmudzi amamdziwa)
Angozo!
Olo mafana amatchula dzina
Amakwana, amathina
Anthu amadziwa ndi makina
Mitu yawo imayima
Angozo ndi Head-cleaner
Dziko limavina
Apapa china nchina
Ngakhale amene sakufuna apange salute
Angozo!

CHORUS
Angozo
Safuna zoyambana Angozo
Angozo
Safuna zokangana Angozo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ndi ntondo ntondo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ntondo

LULU
Angozo mmudzi nkhani ndi yawo
Kulima minda opanda mvula kukolola
Angozo mudzi ukamba za iwo
Mulungu analemba Angozo ngokolola
Ngakhale tsiku la ma dyelero
Azimayi amangofuna Angozo ayimbe ng'oma
Ena akuti ng'omanso ayi
Angozo tiwafuna pafupi ativinitse
Kuntero Ngozo ng'oma kuti Booo
(Ngozo ayimbe ng'oma oh oh)
Kuntero ngozo stepe kuti seee
(Ngozo ayimbe ng'oma oh oh)
Kuntero Ngozo ng'oma kuti Booo
(Ngozo ayimbe ng'oma oh oh)
Kuntero ngozo stepe kuti seee
(Ngozo ayimbe ng'oma oh oh)
Angozo amuna anzawo nsanje
Angozo modzichepetsa kuseka
Angozo sangamalize chitelera
Kuopa kuwadikira pa njira

CHORUS
Angozo
Safuna zoyambana Angozo
Angozo
Safuna zokangana Angozo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ndi ntondo ntondo
Angozo Angozo Angozo
Ndi ntondo ntondo
×



Lyrics taken from /lyrics/p/piksy/angozo.html

  • Email
  • Correct
Submitted by Langwan_Piksy

Angozo meanings

Write about your feelings and thoughts about Angozo

Know what this song is about? Does it mean anything special hidden between the lines to you? Share your meaning with community, make it interesting and valuable. Make sure you've read our simple tips.
U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

Post meanings

U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

official video

Featured lyrics

0-9 A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z