Maso lyrics by Langwan Piksy with meaning. Maso explained, official 2024 song lyrics | LyricsMode.com
Request & respond explanations
  • Don't understand the meaning of the song?
  • Highlight lyrics and request an explanation.
  • Click on highlighted lyrics to explain.
Langwan Piksy – Maso lyrics
Verse 1
Ndakhalilidwa
Ndakankhidwa
Ndakanidwa
Ndasalidwa
Ndapanidwa
But I didn’t go down
Yeah ena ankati sindingazithe
Malo ena sinnapite
Zinawawa koma look at me now
Ey
You know, nthawi zina tima manga ndende tokha
Zabwino zochulukitsa tokha tima blocker
Timafuna zophweka zikavuta tima dropper
Kudikira ena ayambe ife tingokopa
Anthu ochuluka they wanna see me begging
Kuyamba ngati othandiza they wanna leave me hanging
Pankhope ngati a chifundo but I know they faking
Pankhope a chikondi kumbaliko nde ndisekeni
People take your kindness for a weakness
Kusiya zawo uko they mind your business
You know, sometimes ndi bwino kumasunga chinsinsi
Kukhala wekha bola mu mtima wako muli peace
(amen)

Chorus

So many things I can thank god for
Madalitso ndaona ndi maso
Anali nane pompo
Pomwe panali khoma anayikapo khomo
Yeah
So many things I can thank God for
Madalitso ndawaona ndi maso
Zomwe ankati sizingandichitikire
Ndaziona ndi maso

Verse 2
Musanandide mufunse komwe ndachoka
Mukanakhala ine ena a inu mukanafoka
I lost hope
It got too hard to cope
Everything felt so wrong
Man it’s been…. Hard for me
Maloto far from real
Lero mphamvu ndzipeza ain no stopping me
Ndingati ku maloto nkamaona success
Onse munayima nane nyengo iyi God bless
Whoever thought ndidzafika this far?
Ndinali mnyamata pano ndi Mister
Anthu ochuluka callin’ me star
Nsanje ayi mudzinditcha victor
Lero zinthu zimasintha when I step in
Mphepo ingadze molimba I'm not shaken
Ndimangoseka
Zikuphweka
Mulungu wadalitsa zonse zongotheka

Chorus
So many things I can thank god for
Madalitso ndaona ndi maso
Anali nane pompo
Pomwe panali khoma anayikapo khomo
Yeah
So many things I can thank God for
Madalitso ndawaona ndi maso
Zomwe ankati sizingandichitikire
Ndaziona ndi maso

Verse 3
Anthu amene andikondane zeni zeni
(ndawaona ndi maso)
Adani anga onse ali pa ntetete
(ndawaona ndi maso)
Chisomo chanu position kuchita maintain
(ndachiona ndi maso)
Chikondi ndachiona ndi maso…maso…maso

Chorus

So many things I can thank god for
Madalitso ndaona ndi maso
Anali nane pompo
Pomwe panali khoma anayikapo
khomo
Yeah
So many things I can thank God for
Madalitso ndawaona ndi maso
Zomwe ankati sizingandichitikire
Ndaziona ndi maso
×



Lyrics taken from /lyrics/l/langwan_piksy/maso.html

  • Email
  • Correct
Submitted by Langwan_Piksy

Maso meanings

Write about your feelings and thoughts about Maso

Know what this song is about? Does it mean anything special hidden between the lines to you? Share your meaning with community, make it interesting and valuable. Make sure you've read our simple tips.
U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

Post meanings

U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

official video

0-9 A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z